Download PDF
Back to stories list

Khalai akamba ndi Zomela Khalai azungumza na mimea

Written by Ursula Nafula

Illustrated by Jesse Pietersen

Translated by David Sani Mwanza

Read by Christine Mwanza

Language Nyanja

Level Level 2

Narrate full story The audio for this story is currently not available.


Uyu ndi Khalai. Ali ndi zaka zisanu ndi ziwiri. Dzina lake litanthauza kuti “wabwino” mucilankhulo chake, Lubukusu.

Khalai ni msichana mwenye umri wa miaka saba. Jina lake lina maana ya ‘aliye mzuri’ katika lugha yake ya Lubukusu.


Khalai amauka ndikukmba ndi mtengo wa malalanje. “Chonde, mtengo wamalalanje, kula ndipo utipatse malalanje ambiri akupsya”.

Khalai anaamka na kuongea na mmea mchanga wa Mchungwa, “Tafadhali mti wa Mchungwa, kua mkubwa uzae machungwa mengi mabivu.”


Khali ayenda ku sukulu. Pa njira, akamba ndi msipu. “Chonde, kula msipu ndikukhala obiliwira ndipo musaume.”

Khalai anaenda shuleni na njiani anaongea na Nyasi, “Tafadhali Nyasi, kua kijani zaidi na zaidi na wala usikauke.”


Khalai apita pa maluwa amthengo. “Chonde, maluwa, pitilizani kukula kuti ndikuikeni mu tsitsi langa.”.

Khalai anayapita Maua ya mwituni na kusema, “Tafadhali Maua, endelea kunawiri ili niweze kukuweka kwenye nywele zangu.”


Ku sukulu, Khalai akamba ndi mtengo pakati pa sukulu. “Chonde mtengo, khalani ndi nthambi zikulu kuti tiziwerengera pa pansi pa mtengo.

Akiwa shuleni, Khalai anazunguumza na Mti ulioko katikati ya shule, “Tafadhali Mti, toa matawi makubwa ili tusome chini ya kivuli chako.”


Khalai akamba ndi chitseko chakusukulu. “Chonde, kulani olimba ndiponso osalola anthu oipa kti alowe.

Khalai anazunguumza na ua unaoizingira shule yake, “Tafadhali ua, kuwa mwenye nguvu ili uzuie shule yetu kutokana na watu wabaya.”


Pamene Khalai abwelera kunyumba, ayendera mtengo walalanje. “Kodi malalanje ako apsya kale?”. Afunsa Khalai.

Anaporudi nyumbani alasiri, Khalai anautembelea mti wa Mchungwa kuangalia kama machungwa yameiva.


Malalanje akalibe kupya,” anena Khalai. “Mwina, uzandikhalira ndi lalanje lakupya”.

“Machungwa bado mabichi,” Khalai anashusha pumzi. “Nitakuona kesho, we mti wa machungwa. Labda utanipa chungwa bivu wakati huo.”


Written by: Ursula Nafula
Illustrated by: Jesse Pietersen
Translated by: David Sani Mwanza
Read by: Christine Mwanza
Language: Nyanja
Level: Level 2
Source: Khalai talks to plants from African Storybook
Creative Commons License
This work is licensed under a Creative Commons Attribution 4.0 International License.
Options
Back to stories list Download PDF