Descargar PDF
Regresar a lista de cuentos

Nyimbo ya Sakima La canción de Sakima

Texto Ursula Nafula

Ilustraciones Peris Wachuka

Translated by Sitwe Benson Mkandawire

Lectura en voz alta Christine Mwanza

Lengua chinyanja

Nivel Nivel 3

Contar el cuento completo El audio no está disponible actualmente.


Sakima anali kukhala ndi makolo ake ndi mlongo wake wa zaka zakubadwa zinai. Anakhala pa malo a munthu wolemela, Nyumba yao inali ya uzu pothera pa mzere wa mitengo.

Sakima vivía con sus padres y su hermana de cuatro años de edad. Vivían en el terreno de un hombre rico. Su choza de paja estaba al final de una fila de árboles.


Pamene Sakima anali ndi zaka zitatu, anadwala ndipo anakhala wa khungu. Sakima anali ndi matalanta.

Cuando Sakima tenía tres años de edad, se enfermó y perdió la vista. Sakima era un chico talentoso.


Sakima anali kukwanisa kuchita zinthu zambiri zomwe ana a zaka 6 sankakwanisa kuchita.Mwachisanzo, anali kukhala ndi anthu akalu a m’mudzi ndi kukamba zinthu zofunikira.

Sakima hacía muchas cosas que los otros chicos de seis años no podían hacer. Por ejemplo, podía sentarse con los miembros mayores de la aldea y discutir asuntos importantes.


Makolo a Sakima anali kusewenza pa nyumba ya bambo wolemera. Anachoka panyumba m’mamawa ndi kubwelela kunyumba. Sakima anali kukhala ndi mlongo wake.

Los padres de Sakima trabajaban en la casa del hombre rico. Salían a trabajar temprano en la mañana y volvían a casa tarde por la noche. Sakima se quedaba con su hermana pequeña.


Sakima anakonda kuimba nyimbo. Tsiku lina, amai ake anamufunsa, “kodi uphunzila kuti nyimbo izi, Sakima?”

A Sakima le encantaba cantar. Un día su madre le preguntó, “¿Dónde aprendes estas canciones, Sakima?”


Sakima anayankha, “zimabwela chabe, amai. Ndimazimvela m’mutu mwanga ndipo ndimaziimba.”

Sakima le respondió, “Simplemente llegan, madre. Las escucho en mi cabeza y después las canto.”


Sakima anakonda kuimbila mlongo wake wam’gono, makamaka ngati anali wokwiya. Mlongo wake anamvelera ku nyimbo yake yapa mtima. Anatothozedwa.

A Sakima le gustaba cantarle a su hermana pequeña, especialmente cuando ella tenía hambre. Su hermana le escuchaba cantar la canción favorita de Sakima. Y se relajaba bailando con su canción.


“Imbanso, Sakima,” mlongo wake anamupempha. Sakima ankavomela ndi kuimbanso mobwelezera.

“¿Podrías cantarla una y otra vez, Sakima?”, le suplicaba su hermana. Sakima asentía y le cantaba una y otra vez.


Tsiku lina pamene makolo ake anbwelera ku nyumba, anakhala chete. Sakima anadziwa kuti kunali vuto.

Una noche después del trabajo, sus padres volvieron muy callados. Sakima sabía que algo estaba mal.


“Kodi nichani chalakwika, amai, atate?” sakima anafunsa. Sakima anamvela kuti mwana wa bambo wolemera anasowa ndi bambo wake anali ndi chisoni.

“¿Cuál es el problema, madre, padre?” Preguntó Sakima. Sakima se enteró que el hijo del hombre rico se había perdido. El hombre se sentía muy triste y solo.


“Ndingawaimbile. Angakondwelenso,” Sakima anaudza makolo ake. Koma makolo ake sanamuvokeze naye. “Ndi munthu wolemela kwambiri. Iwe uli wa khungu chabe. Uganiza kuti nyimbo yako izamuthandiza?”

“Yo puedo cantar para él. Quizá eso lo hará feliz,” le dijo Sakima a sus padres. Pero sus padres lo desestimaron. “Él es muy rico. Tú sólo eres un chico ciego. ¿Crees que tu canción lo va a ayudar?”


Angakhale choncho, Sakima sanaleke. Mlongo wake wamng’ono anamupasa mphamvu. Iye anati, “Nyimbo za Sakima zimandilimbikitsa pamene ndili okwiya. Zizalimbikitsanso bambo wolemela.

Pero Sakima no se rindió. Su hermana pequeña lo apoyó. Le dijo: “Las canciones de Sakima me ayudan cuando tengo hambre. Van a tranquilizar al hombre rico también.”


Tsiku lotsatilapo, Sakima anapempha mlongo wake kumupeleka ku nyumba ya bambo wolemela.

Al día siguiente, Sakima le pidió a su hermana pequeña que lo llevara a la casa del hombre rico.


Anaimilila pa pafupi ndi dzenera ndi kuyamba kimba nyimbo yake yapa mtima. Posachedwa, mutu wa bambo wolemela unayamba kuonekela pa dezenera lalikulu.

Se paró debajo de una gran ventana y empezó a cantar su canción favorita. Lentamente, el hombre rico comenzó a asomar su cabeza por la gran ventana.


Anchito analeka zomwe anali kuchita. Anamvesela ku nyimbo ya Sakima yabwino. Koma bambo wina anati, “Kulibe omwe anakwanisapo kutonthoza akulu anchito. Kodi mnyamata wakhungu uyu aganiza kuti azawatonthoza?”.

Los trabajadores dejaron de hacer sus tareas. Escucharon la hermosa canción de Sakima. Pero un hombre dijo, “Nadie ha podido consolar al jefe. ¿Acaso este chico ciego cree que él puede consolarlo?”


Sakima anasiliza kuimba nyimbo yake ndipo anatembenuka kufuna kubwelela kunyumba. Koma bambo wolemela atuluka naumuuza nati, “Chonde, imbanso nyimbo.”

Sakima terminó de cantar y se dio vuelta para irse. Pero el hombre rico salió de prisa y dijo: “Por favor canta de nuevo.”


Pa nthawi yomweyo, amuna awiri anabwela apo anyamula munthu. Anali anapeza mwana wa bambo wolemelayo atamenyedwa ndi kusiyidwa pambali pa mseu.

En ese mismo momento, llegaron dos hombres que llevaban a alguien en una camilla. Habían encontrado al hijo del hombre rico apaleado y tirado a un lado del camino.


Bambo wolemela anakondwela kwambiri kuona mwana wake. Anapasa mphaso kwa Sakima powatonthoza. Anapeleka mwana wao ndi Sakima ku chipatala kuti Sakima akayambe kuonanso.

El hombre rico estaba muy feliz de ver a su hijo otra vez. Y le dio una recompensa a Sakima por consolarlo. Llevó a su hijo y a Sakima al hospital para que Sakima pudiera recuperar la vista.


Texto: Ursula Nafula
Ilustraciones: Peris Wachuka
Translated by: Sitwe Benson Mkandawire
Lectura en voz alta: Christine Mwanza
Lengua: chinyanja
Nivel: Nivel 3
Fuente: Sakima's song del African Storybook
Licencia Creative Commons
Esta obra está bajo una Creative Commons Atribución 4.0 Internacional.
Opciones
Regresar a lista de cuentos Descargar PDF