M’mudzi wina womangidwa pamatelo a phili la Kenya Kum’mawa kwa Africa, kamtsikana kakang’ono kamagwila nchito m’munda ndi amai ake. Dzina lake anali Wangari.
En una aldea ubicada en la cuesta del Monte Kenia en África del Este, una niña pequeña trabajaba en los campos con su madre. Su nombre era Wangari.
A Wangari le encantaba estar afuera. En el huerto de su familia, ella separaba la tierra con su machete y plantaba pequeñas semillas en la tierra tibia.
Su momento favorito del día era justo después del anochecer. Cuando se ponía muy oscuro y no podía mirar las plantas. Entonces era cuando Wangari sabía que debía regresar a casa. Ella caminaba por los senderos angostos del campo, cruzando los ríos que estaban en su camino.
Wangari anali mwana wocenjela kwambili ndipo anali wofunitsitsa kupita kusukulu kukaphunzila. Koma makolo ake sanafune kuti kamtsikana aka kaphunzile koma kazikhala pa nyumba ndi kugwila ncthito. Pamene Wangari anali ndi zaka zisanu and ziwili, mukulu wake wamwamuna anagonjetsa makolo awo pokambilana kuti Wangari apite kusukulu akaphunzile.
Wangari era una niña astuta y no podía esperar para ir a la escuela. Pero su madre y padre querían que ella se quedara para ayudarlos con los quehaceres del hogar. Cuando cumplió siete años, su hermano mayor convenció a sus padres para que ella fuera a la escuela.
Wangari anakonda kuphunzila kwambili motelo kuti anaphunzila kopitilila kupyolela mkuwelenga mabuku osiyana-siyana. Ndipo anakhoza kwambili pa sukulu motelo kuti anapeza umwayi wokaphunzila ku dziko lakutali la United States of America. Wangari anasangalala kwambili cifukwa anali kufunitsitsa kudziwa zambili zapa dziko lapansi.
¡A ella le gusta aprender! Wangari aprende muy rápido con cada libro que lee. A ella le iba tan bien en la escuela que la invitaron a estudiar en Estados Unidos. ¡Wangari estaba muy entusiasmada! Ella quería aprender más acerca del mundo.
Wangari anaphunzila zinthu zambili pamene anali pa American Univeziti. Anaphunzila pa zomela ndi mumene zimakulila. Zimenezi zinamukumbutsa mumene anali kusewelela ndi abale ake mthunzi ya mitengo mthengo laku-dziko lokongola la Kenya.
En la universidad americana, Wangari aprendió muchas cosas nuevas. Ella estudió sobre las plantas y cómo ellas crecen. Y recordó cómo ella creció: jugando con su hermano bajo la sombra de árboles hermosos en los bosques de Kenia.
Pamene anali kuphunzila tsiku ndi tsiku anazindikila kuti akonda anthu akwao ku Kenya. Anali kufuna kuti anthu kudziko limeneli tsiku lina akapate ufulu ndi mtendele. Pamene anapitiliza ndi maphunzilo ake, anapitiliza kukumbukila kumalo lakwao ku Africa.
Mientras más aprendía, más se daba cuenta de que le encantaba la gente de Kenia. Ella quería que ellos fueran felices y libres. Mientras más aprendía, más recordaba su casa en África.
Anabwelela kudziko lakwao ku Kenya pamane anamaliza maphunzilo ake ndipo nthawi imeneyi dziko la Kenya linali litasintha. Mapulazi akulu akulu anatenga malo ochuluka. Azimai anali kusowa kotheba nkhuni cifukwa mitengo kunalibe. Anthu anali osauka ndipo ana anali kuoneka anjala.
Al finalizar sus estudios, regresó a Kenia. Pero su país había cambiado. Habían granjas enormes que atravesaban todo el territorio. Las mujeres no tenían madera para hacer fogatas para cocinar. La gente era pobre y los niños tenían hambre.
Wangari anali kudziwa cofunika kucita kuti athetsa mabvuto amenewa: anaphunzitsa azimai kubzyala mitengo kucokela kumbewu. Azimai amenewa anayamba kugulitsa mitengo zao zitakula ndikupeza ndalama zosamalila ma banja awo. Cifukwa cacimenechi azimai anakhala wokondwela kwambili ndi Wangari amene anawa thandiza kuti akhale ndi mphanvu komanso olimba.
Wangari sabía qué hacer. Les enseñó a las mujeres a plantar árboles con semillas. Las mujeres vendían los árboles y usaban aquel dinero para cuidar a sus familias. Las mujeres estaban muy contentas. Wangari las había ayudado a sentirse poderosas y fuertes.
Patapita zaka zambili, mitengo imene inabzyalidwa ija, inakula ndi ku panga thengo. Mitsinje inayambanso kukhala ndi madzi. Mbili ya Wangari inafika ponseponse mu Africa. Lelolino, mitengo yamitundu-mitundu mamilyoni tilkuonayi inacokela ku mbewu ya Wangari.
Con el paso del tiempo, los árboles nuevos siguieron creciendo hacia el bosque, y los ríos comenzaron a fluir nuevamente. El mensaje de Wangari se difundió por toda África. Hoy en día, millones de árboles han crecido gracias a las semillas de Wangari.
Wangari había trabajado muy duro. La gente de alrededor del mundo lo notó, y le otorgaron un premio famoso. Se llama Premio Nobel de la Paz ella fue la primera mujer africana en recibirlo.
Wangari anamwalila mu caka ca 2011, koma timamukumbukila tikamaona mtengo wokongola uliwonse mthengo.
Wangari murió el año 2011, pero la podemos recordar cada vez que miramos un hermoso árbol.