Tsiku lina, kunali banja lina lokondwera.
Es war einmal eine glückliche Familie.
Sanali kuyambana. Anali kuthandizila makolo ao panyumba ndi kumunda.
Sie stritten nie miteinander. Sie halfen ihren Eltern im Haus und auf den Feldern.
Koma sanaloledwe kuyenda pafupi ndi moto.
Aber sie durften nicht in die Nähe von Feuer.
Anali kucita nchito iliyonse usiku. Cifukwa anapandidwa ndi chikonga (wax).
Sie mussten all ihre Arbeit nachts verrichten. Denn sie waren aus Wachs!
Koma munyamata umodzi anali kufunisitsa kuyenda muzuwa.
Aber einer der Jungen sehnte sich nach dem Sonnenlicht.
Tsiku lina, kufunisitsa kwake kunayenda pasogolo. Abale ace anamucenjeza…
Eines Tages war die Sehnsucht zu groß. Seine Brüder warnten ihn …
Koma anacedwa! Anasungunuka muzuwa lakupya kwambiri.
Aber es war zu spät! Er schmolz in der heißen Sonne.
Ana achikonga sanakondwele poona m’bale wao asungunika.
Die Wachskinder waren sehr traurig sehen zu müssen, wie ihr Bruder dahin schmolz.
Koma anapangana zocita. Anapanga kanyoni kucoka ku cikonga ca m’bale wao.
Aber sie schmiedeten einen Plan. Sie formten den geschmolzenen Wachsklumpen zu einem Vogel.
Anapeleka kanyoni m’bale wao pamwamba pa phiri.
Sie brachten ihren Vogelbruder auf einen hohen Berg.
Pamene zuwa linacoka, kanyoni kanambululuka nakuimba m’mamawa mu zuwa.
Und als die Sonne aufging, flog er singend davon ins Morgenlicht.