Schaltfläche PDF
Zurück zur Geschichteliste

Mwana wa Bulu Eselskind

Geschrieben von Lindiwe Matshikiza

Illustriert von Meghan Judge

Übersetzt von David Sani Mwanza

Gelesen von Christine Mwanza

Sprache Nyanja

Niveau Niveau 3

Vollständige Geschichte erzählen Zu dieser Geschichte ist noch kein Audio verfügbar.


Kanali kamwana kakakazi kang’ono komwe kanaona chinthu cha maonekedwe odabwisa patali.

Es war ein kleines Mädchen, das zuerst die mysteriöse Gestalt in der Ferne erkannte.


Pamane chinthu chinabwela pafupi, anaona kuti anali mzimai ome anali ndi mimba yaikulu.

Als die Gestalt näher kam, sah sie, dass es eine hochschwangere Frau war.


Mwamanyazi koma mopanda mantha, kamwana kayenda pafupi ndi mzimai. “Tifunika kukhala nao pamozi,” anthu a kamwana kakazi anavomekezana. “Tizamusunga ndi mwana wake bwino-bwino.

Schüchtern, aber tapfer näherte sich das Mädchen der Frau. „Sie soll bei uns bleiben“, entschied das Volk des kleinen Mädchens. „Wir bieten ihr und ihrem Kind Schutz.“


Mwana anali pafupi kubadwa. “Kankha!” “Bwelesani zovimba!” “Water!” “Kankhaaaa!!!”

Das Kind war bald unterwegs. „Press!“, „Bringt Decken!“, „Wasser!“, „Preeeeeeessen!“


Koma pamene anaona mwana wakhanda, aliyense anabwelera m’mbuyo ndi kudabwa. “Bulu?!”

Aber als sie das Baby sahen, sprangen alle erschrocken zurück. „Ein Esel?!“


Aliyense anayamba kukangana. “Tinakamba kuti tizamusunga pamozi ndi mwana wake bwino-bwino, ndipo tizachita motero,” ena anatero. “Koma azatibweretsera soka!” enanso ananena.

Alle fingen an zu streiten. „Wir haben gesagt, wir beschützen Mutter und Kind, und das werden wir auch tun“, sagten die Einen. „Aber das wird uns Unglück bringen!“, sagten die Anderen.


Chifukwa cha icho, mzimai anasala yekha. Anavutika kuganiza zomwe azachita ndi mwana wodabwisa. Anavutika kuganiza kuti azazichita chani.

Und so fand sich die Frau wieder allein. Sie fragte sich, was sie mit diesem sonderbaren Kind anfangen sollte. Sie fragte sich, was sie mit sich selbst anfangen sollte.


Koma pothera, anafunika kuvomela kuti bulu anali mwana wake ndipo anali mai wake.

Aber schließlich musste sie akzeptieren, dass er ihr Kind und sie seine Mutter war.


Tsono, ngati mwana anakhala chimozimozi, ndi thupi ing’ono, zinthu zinakakhalako bwino. Koma bulu anakula ndi kukula kufikila nthawi yomwe sankakhala pa mbuyo pa mai wake. Ndipo mukhalidwe wake unasiyana ndi munthu. Amai ake anli olema nthawi zambili komanso aukali. Nthawi zina, anatuma mwana kuchita nchito zomwe zinafunikila kuchitika ndi nyama.

Nun, wenn das Kind nicht gewachsen wäre, wäre vielleicht alles anders geworden. Aber das Eselskind wuchs und wuchs bis er nicht mehr auf den Rücken seiner Mutter passte. Und egal, wie sehr er sich bemühte, er konnte sich nicht wie ein Mensch benehmen. Seine Mutter war oft müde und frustriert. Manchmal gab sie ihm Arbeit, die für Tiere bestimmt war.


Msokonezo ndi mkwiyo unakula mu mtima wa bulu. Anali kulephela kuchita zilizonse. Analephela kukhali ndi mkhalidwe weni weni. Anali okwiya kotelo kuti, tsiku lina, anamenyesela amai ake pansi.

Verwirrung und Ärger sammelten sich in Esel. Er konnte dies nicht und das nicht tun. Er konnte so und so nicht sein. Er wurde so wütend, dass er eines Tages seine Mutter zu Boden trat.


Bulu anachita manyazi. Anayamba kuthawila kutali komwe angathe kupita.

Esel schämte sich sehr. Er lief davon so weit er konnte.


Pa nthawi yamene analeka kuthawa, unali usiku, Bulu anasowa. “Hee, hyu?” anatelo ku mdima. Anafika pamathelo. Anayamba kusanduka. Anagona mu tulo twatukulu twa mavuto.

Als er aufhörte zu laufen, war es Nacht und Esel hatte sich verlaufen. „Ih Ah?“, flüsterte er in die Dunkelheit. „Ih Ah?“, hörte man ein Echo. Er war allein. Er rollte sich zusammen und fiel in einen tiefen und unruhigen Schlaf.


Bulu anauka ndi kupeza nkhalamba ili kumuyangana. Anayangana mu maso a mdala ndi kuyamba kukhala ndi chiyembekezo.

Als Esel aufwachte, starrte ihn ein alter Mann an. Er blickte dem alten Mann in die Augen und verspürte einen Schimmer Hoffnung.


Bulu afuna kukhala ndi mdala, omwe anamuphunzisa njira zambili zomwe angakhalilemo umoyo. Bulu anamva ndi kuphunzila, chimozi mozi mdala nayenso anamvesera ndi kuphunzila. Anathandizana ndipo anaseka pamozi.

Esel blieb bei dem alten Mann, der ihm verschiedene Überlebenstricks beibrachte. Esel hörte zu und lernte, genau wie der alte Mann. Sie halfen sich gegenseitig und lachten zusammen.


Tssiku lina m’mawa, mdala anapempha Bulu kuti amunyamule kumupeleka pa mwamba pa phiri.

Eines Morgens bat der alte Mann Esel ihn einen Berg hochzutragen.


Pamwamba pa mithambo, anagona. Bulu analota kuti amai ake anli kudwala ndipo anali kumuitana. Ndipo pamene anauka…

Hoch oben in den Wolken schliefen sie ein. Esel träumte, dass seine Mutter krank sei und nach ihm rief. Und als er aufwachte …


Mithambo inachoka pamozi ndi mzake, mdala.

… waren die Wolken zusammen mit seinem Freund, dem alten Mann, verschwunden.


Bulu anaziwa zomwe anafunika kuchita.

Esel wusste endlich, was er zu tun hatte.


Buu anapeza amai ake, okha ali kulilila mwana wao wosowa. Anapenyana kwakanthawi, ndipo anakumbatilana mwamphamvu.

Esel fand seine Mutter, allein und in Trauer um den Verlust ihres Sohnes. Sie blickten einander lange Zeit an. Dann umarmten sich sich sehr fest.


Bulu ndi amai ake akulila pamozi ndi anapeza nzila zosiyanasiyana zokhalilamo pamozi. Pang’ono pang’ono, onse anthu okhala pafupi nao ndi banja lao ayamba kukhala nao pamozi mopanda vuto lenileni.

Das Eselskind und seine Mutter sind sich näher gekommen und haben neue Wege des Zusammenlebens entdeckt. Langsam lassen sich auch andere Familien rings um sie herum nieder.


Geschrieben von: Lindiwe Matshikiza
Illustriert von: Meghan Judge
Übersetzt von: David Sani Mwanza
Gelesen von: Christine Mwanza
Sprache: Nyanja
Niveau: Niveau 3
Quelle: Donkey Child aus African Storybook
Creative Commons Lizenz
Dieses Werk ist unter einer Creative Commons Namensnennung 4.0 Lizenz lizenziert.
Optionen
Zurück zur Geschichteliste Schaltfläche PDF