Téléchargement PDF
Retour à la liste des contes

Nyimbo ya Sakima La chanson de Sakima

Écrit par Ursula Nafula

Illustré par Peris Wachuka

Traduit par Sitwe Benson Mkandawire

Lu par Christine Mwanza

Langue chewa

Niveau Niveau 3

Lire l’histoire en entier L’enregistrement audio de cette histoire est actuellement indisponible.


Sakima anali kukhala ndi makolo ake ndi mlongo wake wa zaka zakubadwa zinai. Anakhala pa malo a munthu wolemela, Nyumba yao inali ya uzu pothera pa mzere wa mitengo.

Sakima vivait avec ses parents et sa petite sœur, qui avait quatre ans. Ils vivaient sur la terre d’un homme riche. Leur hutte à toit de chaume était située au bout d’un rang d’arbres.


Pamene Sakima anali ndi zaka zitatu, anadwala ndipo anakhala wa khungu. Sakima anali ndi matalanta.

Quand Sakima avait trois ans, il est tombé malade et a perdu la vue. Sakima était un garçon avec beaucoup de talent.


Sakima anali kukwanisa kuchita zinthu zambiri zomwe ana a zaka 6 sankakwanisa kuchita.Mwachisanzo, anali kukhala ndi anthu akalu a m’mudzi ndi kukamba zinthu zofunikira.

Sakima faisait beaucoup de choses que d’autres garçons de six ans ne faisaient pas. Par exemple, il pouvait se tenir avec les membres plus âgés du village et discuter de questions importantes.


Makolo a Sakima anali kusewenza pa nyumba ya bambo wolemera. Anachoka panyumba m’mamawa ndi kubwelela kunyumba. Sakima anali kukhala ndi mlongo wake.

Les parents de Sakima travaillaient chez l’homme riche. Ils quittaient leur maison tôt le matin et revenaient tard le soir. Sakima restait seul chez eux avec sa petite sœur.


Sakima anakonda kuimba nyimbo. Tsiku lina, amai ake anamufunsa, “kodi uphunzila kuti nyimbo izi, Sakima?”

Sakima adorait chanter des chansons. Un jour sa mère lui demanda, « Où apprends-tu à chanter ces chansons, Sakima? »


Sakima anayankha, “zimabwela chabe, amai. Ndimazimvela m’mutu mwanga ndipo ndimaziimba.”

Sakima répondit, « Elles me viennent tout simplement, maman. Je les entends dans ma tête et ensuite je chante. »


Sakima anakonda kuimbila mlongo wake wam’gono, makamaka ngati anali wokwiya. Mlongo wake anamvelera ku nyimbo yake yapa mtima. Anatothozedwa.

Sakima aimait chanter pour sa petite sœur, surtout si elle avait faim. Sa sœur l’écoutait chanter sa chanson préférée. Elle se balançait en écoutant la chanson apaisante.


“Imbanso, Sakima,” mlongo wake anamupempha. Sakima ankavomela ndi kuimbanso mobwelezera.

« Peux-tu la chanter encore et encore, Sakima? » le suppliait sa sœur. Sakima acceptait et la chantait encore et encore.


Tsiku lina pamene makolo ake anbwelera ku nyumba, anakhala chete. Sakima anadziwa kuti kunali vuto.

Un soir quand ses parents sont revenus chez eux, ils étaient très tranquilles. Sakima savait qu’il y avait un problème.


“Kodi nichani chalakwika, amai, atate?” sakima anafunsa. Sakima anamvela kuti mwana wa bambo wolemera anasowa ndi bambo wake anali ndi chisoni.

« Qu’est-ce qu’il y a, maman et papa? » Sakima demanda. Sakima apprit que le fils de l’homme riche avait disparu. L’homme était très triste et seul.


“Ndingawaimbile. Angakondwelenso,” Sakima anaudza makolo ake. Koma makolo ake sanamuvokeze naye. “Ndi munthu wolemela kwambiri. Iwe uli wa khungu chabe. Uganiza kuti nyimbo yako izamuthandiza?”

« Je peux chanter pour lui. Il redeviendra peut-être heureux, » dit Sakima à ses parents. Mais ses parents rejetèrent l’idée. « Il est très riche. Tu es seulement un garçon aveugle. Penses-tu vraiment que ta chanson l’aidera? »


Angakhale choncho, Sakima sanaleke. Mlongo wake wamng’ono anamupasa mphamvu. Iye anati, “Nyimbo za Sakima zimandilimbikitsa pamene ndili okwiya. Zizalimbikitsanso bambo wolemela.

Toutefois, Sakima ne démissionna pas. Sa petite sœur l’appuyait. Elle disait, « Les chansons de Sakima me calment quand j’ai faim. Elles calmeront l’homme riche aussi. »


Tsiku lotsatilapo, Sakima anapempha mlongo wake kumupeleka ku nyumba ya bambo wolemela.

Le lendemain, Sakima demanda à sa petite sœur de le mener chez l’homme riche.


Anaimilila pa pafupi ndi dzenera ndi kuyamba kimba nyimbo yake yapa mtima. Posachedwa, mutu wa bambo wolemela unayamba kuonekela pa dezenera lalikulu.

Il se tint sous une grande fenêtre et commença à chanter sa chanson préférée. Lentement, la tête de l’homme riche apparu à la grande fenêtre.


Anchito analeka zomwe anali kuchita. Anamvesela ku nyimbo ya Sakima yabwino. Koma bambo wina anati, “Kulibe omwe anakwanisapo kutonthoza akulu anchito. Kodi mnyamata wakhungu uyu aganiza kuti azawatonthoza?”.

Les ouvriers arrêtèrent ce qu’ils faisaient. Ils écoutèrent la belle chanson de Sakima. Mais un homme dit, « Personne n’a été capable de consoler le patron. Est-ce que ce garçon aveugle pense qu’il pourra le consoler ? »


Sakima anasiliza kuimba nyimbo yake ndipo anatembenuka kufuna kubwelela kunyumba. Koma bambo wolemela atuluka naumuuza nati, “Chonde, imbanso nyimbo.”

Sakima termina de chanter sa chanson et s’apprêtait à partir. Mais l’homme riche sortit en vitesse et dit, « S’il te plaît, chante encore. »


Pa nthawi yomweyo, amuna awiri anabwela apo anyamula munthu. Anali anapeza mwana wa bambo wolemelayo atamenyedwa ndi kusiyidwa pambali pa mseu.

À ce moment, deux hommes sont arrivés en portant quelqu’un sur une civière. Ils avaient trouvé le fils de l’homme riche tabassé et abandonné sur le bord de la route.


Bambo wolemela anakondwela kwambiri kuona mwana wake. Anapasa mphaso kwa Sakima powatonthoza. Anapeleka mwana wao ndi Sakima ku chipatala kuti Sakima akayambe kuonanso.

L’homme riche fut tellement content de revoir son fils. Il récompensa Sakima de l’avoir consolé. Il emmena les deux garçons à l’hôpital pour que Sakima puisse retrouver la vue.


Écrit par: Ursula Nafula
Illustré par: Peris Wachuka
Traduit par: Sitwe Benson Mkandawire
Lu par: Christine Mwanza
Langue: chewa
Niveau: Niveau 3
Source: Sakima's song du Livre de contes africains
Licence de Creative Commons
Ce travail est autorisé sous une licence Creative Commons Attribution 4.0 non transposé.
Options
Retour à la liste des contes Téléchargement PDF