L’enregistrement audio de cette histoire est actuellement indisponible.
M’mudzi wina womangidwa pamatelo a phili la Kenya Kum’mawa kwa Africa, kamtsikana kakang’ono kamagwila nchito m’munda ndi amai ake. Dzina lake anali Wangari.
Dans un village situé sur les flancs du Mont Kenya en Afrique de l’Est, une petite fille travaillait dans les champs avec sa mère. Son nom était Wangari.
Wangari aimait beaucoup être dehors. Dans le potager de sa famille, elle faisait des trous dans le sol avec sa machette. Elle enfouissait des petites graines dans la terre chaude.
Son moment préféré de la journée était juste après le coucher du soleil. Quand il faisait trop nuit pour voir les plantes, Wangari savait qu’il était l’heure de rentrer à la maison. Pour rentrer, elle devait suivre des sentiers étroits à travers champs et traverser des rivières.
Wangari anali mwana wocenjela kwambili ndipo anali wofunitsitsa kupita kusukulu kukaphunzila. Koma makolo ake sanafune kuti kamtsikana aka kaphunzile koma kazikhala pa nyumba ndi kugwila ncthito. Pamene Wangari anali ndi zaka zisanu and ziwili, mukulu wake wamwamuna anagonjetsa makolo awo pokambilana kuti Wangari apite kusukulu akaphunzile.
Wangari était une enfant intelligente et avait hâte d’aller à l’école. Mais sa mère et son père voulaient qu’elle reste à la maison pour les aider. Quand elle eut sept ans, son grand frère persuada ses parents de la laisser aller à l’école.
Wangari anakonda kuphunzila kwambili motelo kuti anaphunzila kopitilila kupyolela mkuwelenga mabuku osiyana-siyana. Ndipo anakhoza kwambili pa sukulu motelo kuti anapeza umwayi wokaphunzila ku dziko lakutali la United States of America. Wangari anasangalala kwambili cifukwa anali kufunitsitsa kudziwa zambili zapa dziko lapansi.
Elle aimait apprendre ! Wangari apprenait de plus en plus avec chaque livre qu’elle lisait. Elle travaillait si bien à l’école qu’elle fut invitée à étudier aux Etats Unis d’Amérique. Wangari était enthousiaste ! Elle voulait en savoir plus sur le monde.
Wangari anaphunzila zinthu zambili pamene anali pa American Univeziti. Anaphunzila pa zomela ndi mumene zimakulila. Zimenezi zinamukumbutsa mumene anali kusewelela ndi abale ake mthunzi ya mitengo mthengo laku-dziko lokongola la Kenya.
A l’université américaine, Wangari apprit beaucoup de choses nouvelles. Elle étudia les plantes et la manière dont elles grandissent. Et elle se rappela comment elle avait grandi : en jouant avec ses frères à l’ombre des arbres dans les magnifiques forêts du Kenya.
Pamene anali kuphunzila tsiku ndi tsiku anazindikila kuti akonda anthu akwao ku Kenya. Anali kufuna kuti anthu kudziko limeneli tsiku lina akapate ufulu ndi mtendele. Pamene anapitiliza ndi maphunzilo ake, anapitiliza kukumbukila kumalo lakwao ku Africa.
Plus elle apprenait, plus elle réalisait qu’elle aimait les habitants du Kenya. Elle voulait qu’ils soient heureux et libres. Plus elle apprenait, plus elle se rappelait son foyer africain.
Anabwelela kudziko lakwao ku Kenya pamane anamaliza maphunzilo ake ndipo nthawi imeneyi dziko la Kenya linali litasintha. Mapulazi akulu akulu anatenga malo ochuluka. Azimai anali kusowa kotheba nkhuni cifukwa mitengo kunalibe. Anthu anali osauka ndipo ana anali kuoneka anjala.
Quand elle eut terminé ses études, elle retourna au Kenya. Mais son pays avait changé. De larges fermes s’étendaient à travers la campagne. Les femmes n’avaient plus de bois pour cuire les aliments. Les gens étaient pauvres et les enfants avaient toujours faim.
Wangari anali kudziwa cofunika kucita kuti athetsa mabvuto amenewa: anaphunzitsa azimai kubzyala mitengo kucokela kumbewu. Azimai amenewa anayamba kugulitsa mitengo zao zitakula ndikupeza ndalama zosamalila ma banja awo. Cifukwa cacimenechi azimai anakhala wokondwela kwambili ndi Wangari amene anawa thandiza kuti akhale ndi mphanvu komanso olimba.
Wangari savait ce qu’il fallait faire. Elle apprit aux femmes comment planter des arbres en utilisant des graines. Les femmes vendirent les arbres et utilisèrent l’argent pour faire vivre leurs familles. Les femmes étaient très heureuses. Wangari les avait aidées à se sentir puissantes et fortes.
Patapita zaka zambili, mitengo imene inabzyalidwa ija, inakula ndi ku panga thengo. Mitsinje inayambanso kukhala ndi madzi. Mbili ya Wangari inafika ponseponse mu Africa. Lelolino, mitengo yamitundu-mitundu mamilyoni tilkuonayi inacokela ku mbewu ya Wangari.
Avec le temps, les nouveaux arbres se transformèrent en forêts, et les rivières recommencèrent à couler. Le message de Wangari traversa toute l’Afrique. Aujourd’hui des millions d’arbres ont grandi grâce aux graines de Wangari.
Wangari avait travaillé dur. Partout dans le monde, les gens s’en aperçurent et lui donnèrent un prix renommé. Il s’appelle le Prix Nobel de la Paix et elle fut la première femme africaine à le recevoir.
Wangari anamwalila mu caka ca 2011, koma timamukumbukila tikamaona mtengo wokongola uliwonse mthengo.
Wangari mourut en 2011 mais nous pensons à elle à chaque fois que nous voyons un bel arbre.