Nkhuku ndi Bongololo anali abwenzi. Koma anali kukonda kupikisana. Tsiku lina, anaganiza kuchaya m’pila wa myendo kuti aone ngati katswili ndi ndani.
Chicken and Millipede were friends. But they were always competing with each other. One day they decided to play football to see who the best player was.
Inkoko ne Ciyongoli fyali fibusa. Nomba lyonse bale cinfyanayafye. Bushiku bumo, baile mukuteya umupila wakumakasa pakuti bamone uwingacinfya umunankwe.
Anayenda kubwalo la m’pila ndipo anayamba masewera awo. Nkhuku inafulumira, koma Bongololo anafulumira kopambana. Nkhuku inachaila kutali koma bongololo anachaila kutali mopambana. Nkhuku inayamba kukalipa.
They went to the football field and started their game. Chicken was fast, but Millipede was faster. Chicken kicked far, but Millipede kicked further. Chicken started to feel grumpy.
Baile kucibansa camupila nokwamba ukuteya. Inkoko yali iya angukilwa nomba iciyongoli calyangukishe ukucilapo. Inkolo epakupantila ukutali nomba iciyongoli tepakupantisha ukucilapo. Inkoko epakwamba ukunfwa ububi.
They decided to play a penalty shoot-out. First Millipede was goal keeper. Chicken scored only one goal. Then it was the chicken’s turn to defend the goal.
As Chicken was walking home, she met Mother Millipede. Mother Millipede asked, “Have you seen my child?” Chicken didn’t say anything.
Mother Millipede was worried.
Amake Bongololo anamva kaliu kakang’ono. “Ndithandizeni amai!”, liu linalila. Amake Bongololo anayangana uku ndi uku, ndi kumvetsetsa ndi cidwi. Mau anacokera mumimba mwa nkhuku.
Then Mother Millipede heard a tiny voice. “Help me mom!” cried the voice. Mother Millipede looked around and listened carefully. The voice came from inside the chicken.