Mutima wanga umvela zinthu zambili.
My heart feels a lot of
things.
Umutima wandi ulomfwa ifintu ifingi.
Ndimvela kukondwela ngati ambuya anga atiuza nthano m’madzulo.
I feel happy when my
granny tells us stories
in the evening.
Ndatemwa nga bamaama baleetushimikila utushimi ubushiku.
Ndimvela kukhala wosangalala ngati ndisewela ndi mzanga.
I feel silly when I play
with my friend.
Ndomfwa ukusaamwa nga ndeyangala no munandi.
Ndimamvela kuipa ngati atate anena kuti alibe ndalama.
I feel bad when my dad
says he does not have
money.
Nshumfwa bwino bataata nga batiila tabakwete indalama.
Ndimvela wokondedwa ngati amai anga andikumbatila.
I feel loved when my
mom gives me a hug.
Ndomfwa ukutemwikwa nga bamaayo bankumbatila.