Tsiku lina, amai anatenga zipatso zambili.
Un día, mamá trajo mucha fruta.
“Ndipotani tingakhale ndi zipatso?” Tifunsa. “Tidzadya zipatso usiku walelo” Anatelo amai.
“¿Cuándo podemos comer fruta?” le preguntamos. “Esta noche comeremos fruta,” dice mamá.
M’bale wanga Rahim ndi ozikonda. Alawa zipatso zonse. Akudya ziphaso zambili.
Mi hermano Rahim es glotón. Prueba toda la fruta. Come mucha.
“Onani zimene Rahim anacita!” Anafuula m’bale wanga wamg’ono. “Rahim ndiwamakani ndiponso ozikonda” Nditelo.
“¡Mira lo que hizo Rahim!” grita mi hermano pequeño. “Rahim es travieso y egoísta,” le respondo.
Amai ndiokalipa na Rahim.
Mamá se enoja con Rahim.
Naifenso ndife okalipa na Rahim. Koma Rahim sapepesa.
Nosotros también nos enojamos con Rahim. Pero Rahim no está arrepentido.
“Kodi simuzamupatsa cilango?” Afunsa m’bale wamng’ono.
“¿No vas a castigar a Rahim?” pregunta mi hermano pequeño.
“Rahim, posacedwa apa, uzacita cisoni,” amucenjeza amai.
“Rahim, pronto te arrepentirás,” le advierte mamá.
Rahim wayamba kumva kudwala.
Rahim empieza a sentir náuseas.
“M’mimba mwanga mwayamba kuwawa,” anong’oza Rahim.
“Me duele mucho el estómago,” susurra Rahim.
Amai anadziwa kuti izi zidzacitika. Cipatso cimupatsa cilango Rahim!
Mamá sabía que esto pasaría. ¡La fruta está castigando a Rahim!
Pambuyo pake, Rahim apepesa kwa ife. “Sindidzakhalanso wozikonda tele,” alonjeza. Ndipo timukhulupilila tonse.
Más tarde, Rahim nos pide disculpas. “No volveré a ser tan glotón,” promete. Y todos aceptamos su promesa.