Suddenly, they realised that it was
late.
They hurried back to the village.
Pamene anali pafupi na nyumba, Nozibele anaika kwanja yake pakhosi. Anaiwala ndendele mwina mkanda wovala pakhosi. Anapempha anzace kuti abwelele kumtsinje kukatenga ndendele. Koma anzace anati kwafipa kwambiri.
When they were nearly home,
Nozibele put her hand to her neck.
She had forgotten her necklace!
“Please come back with me!” she
begged her friends.
But her friends said it was too late.
To her surprise, a dog opened the
door and said, “What do you want?”
“I’m lost and I need a place to
sleep,” said Nozibele.
“Come in, or I’ll bite you!” said the
dog.
So Nozibele went in.
Galu inati, “Ndiphikile” “Sininaphikilepo galu mu umoyo wanga” anatelo Nozibele. “Phika, ngati suphika nizakuluma” Inatelo galu. Nozibele anaphika zakudya zagalu.
Then the dog said, “Cook for me!”
“But I’ve never cooked for a dog
before,” she answered.
“Cook, or I’ll bite you!” said the dog.
So Nozibele cooked some food for
the dog.
Galu inati, “Ndikonzele pogona” Nozibele anati, “Sindinakonzelepo galu pogona mu umoyo wanga” “Ndikonzele pogona, ngati sundikonzela ndizakuluma” Inatelo galu. Nozibele anakonza pogona galu.
Then the dog said, “Make the bed
for me!”
Nozibele answered, “I’ve never
made a bed for a dog.”
“Make the bed, or I’ll bite you!” the
dog said.
So Nozibele made the bed.
Every day she had to cook and
sweep and wash for the dog.
Then one day the dog said,
“Nozibele, today I have to visit
some friends. Sweep the house,
cook the food and wash my things
before I come back.”
Pamane galu inacoka cabe, Nozibele anacosa sisi litatu kucoka kumutu wake. Anaika sisi limodzi pansi pa bedi, yimodzi kumbuyo kwa citseko ndi ina mosungila ng’ombe. Ndiponso iye anathamangila kunyumba mwansanga.
As soon as the dog had gone,
Nozibele took three hairs from her
head.
She put one hair under the bed, one
behind the door, and one in the
kraal.
Then she ran home as fast as she
could.
Pamene Galu inabwelera, inasakila Nozibele. “Nozibele ulikuti?” Anapunda galu. “Nilikuno kunyansi kwa bedi” Sisi loyamba linayankha. “Nilikuno kumbuyo kwa citseko” Sisi laciwiri linayankha. “Nilikuno kosungila ng’ombe” Sisi lacitatu linayankha.
When the dog came back, he looked
for Nozibele.
“Nozibele, where are you?” he
shouted.
“I’m here, under the bed,” said the
first hair.
“I’m here, behind the door,” said the
second hair.
“I’m here, in the kraal,” said the
third hair.
Gulu inaziwa kuti Nozibele athawa. Gala anathamanga kuyenda kumunzi kwa Nozibele. Koma abale a Nozibele anali kuyembekeza ndi tumitengo tukulutukulu. Galu inabwelela nakuthawa ndiponso ikalibe kuonekelanso kucoka paja.
Then the dog knew that Nozibele
had tricked him.
So he ran and ran all the way to the
village.
But Nozibele’s brothers were
waiting there with big sticks.
The dog turned and ran away and
has never been seen since.