Mwamanyazi koma mopanda mantha, kamwana kanasendela pafupi ndi mzimai. “Tifunika kuwasunga,” anthu a kamwana kakazi anaganizila. “Tizamusunga ndi mwana wake bwino-bwino.
Cifukwa ca ico, mzimai anakhalanso yekha. Anabvutika kuganiza zomwe azacita ndi mwana wodabwisa. Anabvutika kuziganizila cocita.
妇女发现自己又孤零零一人了。她不知道该拿这个奇怪的孩子怎么办,她也不知道自己该怎么办。
Koma pothela, anavomela kuti bulu anali mwana wake ndipo anali mai wake.
最后,她决定接受这个孩子,做他的妈妈。
Tsopano, ngati mwana anakhala cimodzimodzi, ndi thupi ing’ono, zinthu zinakakhalako mosiyana. Koma bulu anakula ndi kukula kufikila nthawi yomwe sankakhala pa msana pa mai wake. Ndipo mkhalidwe wake unasiyana ndi munthu. Amai ake anali olema nthawi zamblili komanso aukali. Nthawi zina, anatuma mwana kucita nchito zomwe zinafunikila kucitika ndi nyama.
Pa nthawi imene analeka kuthamanga, unali usiku, Bulu anasowa. “Hee, hyu?” ananong’oneza ku mdima. Anafika pamathelo. Anayamba kusanduka ka bola kokhwima. Anagona mu tulo twatukulu twa mabvuto.