Ndipo Odongo na Apiyo anayenda panja nayamba kupilikisa ma bulaula na mbalame.
欧东格和阿皮尤跑出去玩儿了,他们追着蝴蝶和鸟儿,在它们后面跑。
Ana awa, anakwela mitengo ndipo anasewela m’madzi amnyanja.
他们还爬树,跳进湖里,溅起了很多水花。
Pamene kunada, ana anabwelela kunyumba kukadya cakudya ca madzulo. Koma akalibe kutsiliza kudya, anayamba kumva tulo!
天黑了,他们回到奶奶的家里吃晚饭,但他们太累了,还没吃完,就睡着了。
M’mawa mwake, atate awo a Odongo ndi Apiyo anabwelela ku tauni ndikuwasiya ndi ambuya awo Nyar-Kanyada.
第二天,爸爸开车回城了,把孩子们留给奶奶。
Odongo ndi Apiyo anathandiza ambuya awo nchito za panyumba. Ana awa anatunga madzi ndi kusakila nkhuni. Anatola mazila ankhuku ndi kuthyola ndiyo m’dimba.
欧东格和阿皮尤帮助奶奶做家务。他们帮奶奶拎水,运柴。他们还帮奶奶从鸡窝里拿鸡蛋,在花园里摘蔬菜。
Ambuya awo anapunzisa adzukulu awo kuphika nsima, nsomba, ndi ndiyo zina zakumudzi.
Tsiku linanso, ana anapitaa ku musika ndi ambuya awo. Anali ndi stolo yogulitsamo ndiyo za m’munda, shuga ndi sopo. Apiyo anali kukonda kuuza anthu ogula mitengo ya zinthu. Odongo anali kukonda kulongeza zinthu zimene anthu anali kugula.
Odongo ndi Apiyo anakumbatilana nao ambuya awo nalayilana.
欧东格和阿皮尤紧紧地抱着她,跟她告别。
Pamene Odongo nda Apiyo anabwelela kusukulu, anauza anzao za umoyo wakumudzi. Ana ena anadziwa kuti umoyo wa mtauni ndi wabwino. Ena anakonda umoyo wakumudzi. Koma ambili a iwo, onse ananena kuti ambuya a Odongo ndi Apiyo anali abwino mtima!